Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 13:6-8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. Ndipo panali atapita masiku ambiri, kuti Yehova anati kwa ine, Uka, pita ku Firate, nukatenge kumeneko mpango uja, ndinakuuza iwe ukaubise kumeneko.

7. Ndipo ndinanka ku Firate, ndikumba, nditenga mpango m'malo m'mene ndinaubisamo; ndipo, taonani, mpango unaonongeka, wosayenera kanthu.

8. Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, kuti,

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 13