Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 13:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo panali atapita masiku ambiri, kuti Yehova anati kwa ine, Uka, pita ku Firate, nukatenge kumeneko mpango uja, ndinakuuza iwe ukaubise kumeneko.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 13

Onani Yeremiya 13:6 nkhani