Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 12:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma inu, Yehova, mundidziwa ine; mundiona ine, muyesa mtima wanga ngati utani nanu; muwaturutse iwo monga nkhosa za kuphedwa, ndi kuwakonzeratu tsiku lakuphedwa.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 12

Onani Yeremiya 12:3 nkhani