Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 11:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti ndinatsimikizitsa kwa atate anu tsiku lomwe ndinawaturutsa iwo ku dziko la Aigupto, mpaka lero lomwe, kuuka mamawa ndi kutsimikiza, kuti, Mverani mau anga.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 11

Onani Yeremiya 11:7 nkhani