Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 11:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

kuti ndikalimbikitse lumbiro limene ndinalumbirira makolo anu, ndiwapatse dziko mayenda mkaka ndi uci, monga lero lomwe. Ndipo ndinayankha, ndi kuti, Amen, Yehova.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 11

Onani Yeremiya 11:5 nkhani