Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Rute 2:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nati Naomi kwa mpongozi wace, Yehova amdalitse amene sanaleka kuwacitira zokoma amoyo, ndi akufa. Ndipo Naomi ananena baye, Munthuyu ndiye mbale wathu, ndiye mmodzi wa iwo otiombolera colowa.

Werengani mutu wathunthu Rute 2

Onani Rute 2:20 nkhani