Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Oweruza 9:55-57 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

55. Pamene amuna a Israyeli anaona kuti adafa Abimeleki anamuka yense kumalo kwace.

56. Momwemo Mulungu anambwezera Abimeleki coipaco anacitira atate wace ndi kuwapha abale ace makumi asanu ndi awiri.

57. Ndipo Mulungu anawabwezera coipa conse ca amuna a ku Sekemu pamitu pao, ndipo linawagwera temberero la Yotamu mwana wa Yerubaala.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 9