Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Oweruza 21:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Natiiwo, Taonani, pali madyerero a Yehova caka ndi caka ku Silo, ndiko kumpoto kwa Beteli, kum'mawa kwa mseu wokwera kucokera ku Beteli kumka ku Sekemu, ndi kumwela kwa Lebona.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 21

Onani Oweruza 21:19 nkhani