Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Oweruza 14:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo analira pamaso pace masiku asanu ndi awiriwo pocitika madyerero ao; koma kunali kuti tsiku lacisanu ndi ciwiri anamuuza, popeza anamuumiriza; ndipo anatanthauzira anthu a mtundu wace mwambiwo.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 14

Onani Oweruza 14:17 nkhani