Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Obadiya 1:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. MASOMPHENYA a Obadiya. Atero Ambuye Yehova za Edomu: Tamva mbiri yocokera kwa Yehova, ndi mthenga wotumidwa mwa amitundu, ndi kuti, Nyamukani, timuukire kumthira nkhondo.

2. Taona, ndakuika wamng'ono mwa amitundu; unyozedwa kwambiri.

3. Kudzikuza kwa mtima wako kwakunyenga, iwe wokhala m'mapanga a thanthwe, iwe pokhala pako pamwamba, wakunena m'mtima mwace, Adzanditsitsira pansi ndani?

Werengani mutu wathunthu Obadiya 1