Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Obadiya 1:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kudzikuza kwa mtima wako kwakunyenga, iwe wokhala m'mapanga a thanthwe, iwe pokhala pako pamwamba, wakunena m'mtima mwace, Adzanditsitsira pansi ndani?

Werengani mutu wathunthu Obadiya 1

Onani Obadiya 1:3 nkhani