Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 36:9-13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

9. Motero colowa ca ana a Israyeli sicidzamka m'pfuko m'pfuko, pakuti mapfuko a ana a Israyeli adzamamatira lonse ku colowa cace cace.

10. Monga Yehova adalamulira Mose, momwemo ana akazi a Tselofekadi anacita;

11. popeza Mala, Tiriza, ndi Hogila, ndi Milika, ndi Nowa, ana akazi a Tselofekadi, anakwatibwa ndi ana amuna a abale a atate wao.

12. Anakwatibwa mwa mabanja a ana a Manase mwana wa Yosefe; ndipo colowa cao dnakhala m'pfuko la banja la atate wao.

13. Awa ndi malamulo ndi maweruzo, amene Yehova analamulira ana a Israyeli ndi dzanja la Mose m'zidikha za Moabu pa Yordano ku Yeriko.

Werengani mutu wathunthu Numeri 36