25. Wa pfuko la ana a Zebuloni, kalonga Elisafana mwana wa Paranaki.
26. Wa pfuko la ana a Isakara, kalonga Palitiyeli mwana wa Azana.
27. Wa pfuko la ana a Aseri, kalonga Ahihudi mwana wa Selomi.
28. Wa pfuko la ana a Nafitali, kalonga Pedaheli mwana wa Amihudi.
29. Iwo ndiwo amene Yehova analamulira agawire ana a Israyeli colowa cao m'dziko la Kanani.