21. Wa pfuko la Benjamini, Elidadi mwana wa Kisiloni.
22. Wa pfuko la ana a Dani, kalonga Buki mwana wa Yogili.
23. Wa ana a Yosefe; wa pfuko la ana a Manase, kalonga Haniyeli mwana wa Efodi.
24. Wa pfuko la ana a Efraimu, kalonga Kemuyeli mwana wa Sipitana.