20. Wa pfuko la ana a Simeoni, Semuyeli mwana wa Amihudi.
21. Wa pfuko la Benjamini, Elidadi mwana wa Kisiloni.
22. Wa pfuko la ana a Dani, kalonga Buki mwana wa Yogili.
23. Wa ana a Yosefe; wa pfuko la ana a Manase, kalonga Haniyeli mwana wa Efodi.
24. Wa pfuko la ana a Efraimu, kalonga Kemuyeli mwana wa Sipitana.
25. Wa pfuko la ana a Zebuloni, kalonga Elisafana mwana wa Paranaki.
26. Wa pfuko la ana a Isakara, kalonga Palitiyeli mwana wa Azana.
27. Wa pfuko la ana a Aseri, kalonga Ahihudi mwana wa Selomi.
28. Wa pfuko la ana a Nafitali, kalonga Pedaheli mwana wa Amihudi.
29. Iwo ndiwo amene Yehova analamulira agawire ana a Israyeli colowa cao m'dziko la Kanani.