Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 31:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anapha mafumu a Amidyani pamodzi ndi ophedwa ao ena; ndiwo Evi, ndi Rekamu, ndi Zuri, ndi Huri, ndi Reba, mafumu asanu a Amidyani; namupha Balamu mwana wa Beori ndi lupanga.

Werengani mutu wathunthu Numeri 31

Onani Numeri 31:8 nkhani