Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 31:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anadza nao andende, ndi zakunkhondo, ndi zofunkha, kwa Mose, ndi kwa Eleazara wansembe, ndi kwa khamu la ana a Israyeli, kucigono, ku zidikha za Moabu, ziri ku Yordano pafupi pa Yeriko.

Werengani mutu wathunthu Numeri 31

Onani Numeri 31:12 nkhani