Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 27:3-6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. Atate wathu adamwalira m'cipululu, ndipo sanakhala iye pakati pa msonkhano wa iwo akusonkhana kutsutsana ndi Yehova, mu msonkhano wa Kora; koma anafera zoipa zace zace; ndipo analibe ana amuna.

4. Licotsedwerenji dzina la atate wathu pakati pa banja lace, popeza alibe mwana wamwamuna? Tipatseni dziko lathu lathu pakati pa abale a atate wathu.

5. Ndipo Mose anapita nao mlandu wao pamaso pa Yehova.

6. Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,

Werengani mutu wathunthu Numeri 27