Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 26:13-17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

13. Zera, ndiye kholo la banja la Azera; Sauli, ndiye kholo la banja la Asauli.

14. Iwo ndiwo mabanja a Asimeoni, zikwi makumi awiri mphambu ziwirikudzamazana awiri.

15. Ana amuna a Gadi monga mwa mabanja ao ndiwo: Zefoni, ndiye kholo la banja la Azefoni; Hagi, ndiye kholo la banja la Ahagi; Suni, ndiye kholo la banja la Asuni;

16. Ozini, ndiye kholo la banja la Aozini; Eri, ndiye kholo la banja la Aeri;

17. Arodi, ndiye kholo la banja la Aarodi; Areli, ndiye kholo la banja la Aareli.

Werengani mutu wathunthu Numeri 26