Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 22:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Moabu anati kwa akuru a Midyani, Tsopano msonkhano uwu udzanyambita zonse ziri pozinga pathu, monga ng'ombe zinyambita msipu wa kubusa. Ndipo Balaki mwana wa Zipori anali mfumu ya Moabu masiku amenewo.

Werengani mutu wathunthu Numeri 22

Onani Numeri 22:4 nkhani