Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 10:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pamene mupita kunkhondo m'dziko lanu kucita nkhondo pa mdani wakusautsa inu, mulize cokweza ndi malipenga; ndipo Yehova Mulungu wanu adzakumbukila inu, nadzakupulumutsani kwa adani anu.

Werengani mutu wathunthu Numeri 10

Onani Numeri 10:9 nkhani