Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 9:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo munampeza mtima wace wokhulupirika pamaso panu, nimunapangana naye kumpatsa dziko la Akanani, Ahiti, Aamori, ndi Aperizi, ndi Ayebusi, ndi Agirigasi, kulipereka kwa mbumba zace; ndipo mwakwaniritsa mau anu, popeza Inu ndinu wolungama.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 9

Onani Nehemiya 9:8 nkhani