Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 9:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Inu ndinu Yehova, nokhanu; mwalenga thambo, kumwambamwamba, ndi khamu lao lonse, dziko lapansi, ndi zonse ziri pomwepo, nyanja ndi zonse ziri m'mwemo, ndi Inu muzisunga zamoyo zonsezi, ndi khamu la kumwamba lilambira Inu.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 9

Onani Nehemiya 9:6 nkhani