Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 8:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndi kuti azilalikira ndi kumveketsa m'midzi mwao monse ndi m'Yerusalemu, ndi kuti, Muziturukira kuphiri, ndi kutengako nthambi za azitona, ndi nthambi za mitengo yamafuta, ndi nthambi za mitengo yamcisu, ndi zinkhwamba za migwalangwa, ndi nthambi za mitengo zothonana, kumanga nazo misasa monga munalembedwa.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 8

Onani Nehemiya 8:15 nkhani