Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 7:70 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ena a akuru a nyumba za makolo anapereka kunchito. Kazembeyo anapereka kucuma madariki agolidi cikwi cimodzi, mbale zawazira makumi asanu, maraya a ansembe makumi atatu.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 7

Onani Nehemiya 7:70 nkhani