Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 5:17-19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

17. Panalinso podyera ine Ayuda ndi olamulira amuna zana limodzi; mphambu makumi asanu, pamodzi ndi iwo akutidzera kucokera kwa amitundu otizinga.

18. Zokonzekeratu tsiku limodzi tsono ndizo ng'ombe imodzi, ndi nkhosa zonenepa zisanu ndi imodzi, anandikonzeratunso nkhuku, ndi kamodzi atapita masiku khumi vinyo wambiri wa mitundu mitundu; cinkana conseci sindinafunsira cakudya ca kazembe, popeza ukapolo unalemerera anthuwo.

19. Mundikumbukire Mulungu, zindikomere zonse ndinacitira anthu awa.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 5