Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 3:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Potsatizana naye anakonza Alevi, Rehumu mwana wa Bani. Pambali pace anakonza Hasabiya mkuru wa dera lina la dziko la Keila, kukonzera dziko lace.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 3

Onani Nehemiya 3:17 nkhani