Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 12:44 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo tsiku lomwelo anaika anthu asunge zipinda za cuma, za nsembe zokweza, za zipatso zoyamba, ndi za limodzi limodzi la magawo khumi, kulonga m'mwemo, monga mwa minda ya midzi, magawo onenedwa ndi cilamulo, akhale a ansembe ndi Alevi; popeza Yuda anakondwera nao ansembe ndi Alevi lakuimirirako.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 12

Onani Nehemiya 12:44 nkhani