Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 10:39 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti ana a Israyeli ndi ana a Levi, azibwera nayo nsembe yokweza yatirigu, ndi yavinyo ndi yamafuta, kuzipinda kuli zipangizo za malo opatulika, ndi ansembe akutumikira, ndi odikira, ndi oyimbira; kuti tisasiye nyumba ya Mulungu wathu.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 10

Onani Nehemiya 10:39 nkhani