Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 10:38 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo wansembe mwana wa Aroni azikhala ndi Alevi, polandira Alevi limodzi limodzi la magawo khumi; ndi Alevi azikwera nalo limodzi la magawo khumi mwa limodzi limodzi la magawo khumi ku nyumba ya Mulungu wathu, kuzipinda, ku nyumba ya cuma.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 10

Onani Nehemiya 10:38 nkhani