Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mlaliki 11:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kondwera ndi unyamata wako, mnyamata iwe; mtima wako nukasangalale masiku a unyamata wako, nuyende m'njira za mtima wako, ndi monga maso ako aona; koma dziwitsa kuti Mulungu adzanena nawe mlandu wa zonsezi.

Werengani mutu wathunthu Mlaliki 11

Onani Mlaliki 11:9 nkhani