Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Miyambi 8:34-36 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

34. Ngwodala amene andimvera, nadikira pa zitseko zanga tsiku ndi tsiku,Ndi kulinda pa mphuthu za makoma anga;

35. Pakuti wondipeza ine apeza moyo;Yehova adzamkomera mnma.

36. Koma wondicimwira apweteka moyo wace;Onse akundida ine akonda imfa.

Werengani mutu wathunthu Miyambi 8