33. Imvani mwambo, mukhale anzeru osaukana.
34. Ngwodala amene andimvera, nadikira pa zitseko zanga tsiku ndi tsiku,Ndi kulinda pa mphuthu za makoma anga;
35. Pakuti wondipeza ine apeza moyo;Yehova adzamkomera mnma.
36. Koma wondicimwira apweteka moyo wace;Onse akundida ine akonda imfa.