Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Miyambi 3:1-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Mwananga, usaiwale malamulo anga,Mtima wako usunge malangizo anga;

2. Pakuti adzakuonjezera masiku ambiri,Ndi zaka za moyo ndi mtendere.

3. Cifundo ndi coonadi zisakusiye;Uzimange pakhosi pako;Uzilembe pamtima pako;

4. Motero udzapezakisomo ndi nzeru yabwino,Pamaso pa Mulungu ndi anthu.

5. Khulupirira Yehova ndi mtima wako wonse,Osacirikizika pa luntha lako;

Werengani mutu wathunthu Miyambi 3