14. Omwe asangalala pocita zoipa,Nakondwera ndi zokhota zoipa;
15. Amene apotoza njira zao,Nakhotetsa mayendedwe ao;
16. Nzeru idzakupulumutsa kwa mkazi waciwerewere,Kwa mkazi wacilendo wosyasyalika ndi mau ace;
17. Wosiya bwenzi la ubwana wace,Naiwala cipangano ca Mulungu wace;