6. M'nyumba ya wolungama muli katundu wambiri;Koma m'phindu la woipa muli bvuto,
7. Milomo ya anzeru iwanditsa nzeru,Koma mtima wa opusa suli wolungama.
8. Nsembe ya oipa inyansa Yehova;Koma pemphero la oongoka mtima limkondweretsa.
9. Njira ya oipa inyansa Yehova;Koma akonda wolondola cilungamo.
10. Wosiya njira adzalangidwa mowawa;Wakuda cidzudzulo adzafa.