Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Miyambi 15:6-10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. M'nyumba ya wolungama muli katundu wambiri;Koma m'phindu la woipa muli bvuto,

7. Milomo ya anzeru iwanditsa nzeru,Koma mtima wa opusa suli wolungama.

8. Nsembe ya oipa inyansa Yehova;Koma pemphero la oongoka mtima limkondweretsa.

9. Njira ya oipa inyansa Yehova;Koma akonda wolondola cilungamo.

10. Wosiya njira adzalangidwa mowawa;Wakuda cidzudzulo adzafa.

Werengani mutu wathunthu Miyambi 15