30. Kuunika kwa maso kukondweretsa mtima;Ndipo pomveka zabwino mafupa amatenga uwisi.
31. Khutu lomvera cidzudzulo ca moyoLidzakhalabe mwa anzeru.
32. Wokana mwambo apeputsa moyo wace;Koma wosamalira cidzudzulo amatenga nzeru.
33. Kuopa Yehova ndiko mwambo wanzeru;Ndipo cifatso citsogolera ulemu.