18. Munthu wozaza aputa makani;Koma wosakwiya msanga atonthoza makangano.
19. Mayendedwe a wolesi akunga Hnga laminga,Koma njira ya oongoka mtima iundidwa ngati mseu.
20. Mwana wanzeru akondweretsa atate wace;Koma munthu wopusa apeputsa amace.
21. Wosowa nzeru akondwera ndi utsiru;Koma munthu wozindikira aongola mayendedwe ace.
22. Zolingalira zizimidwa popanda upoKoma pocuruka aphungu zikhazikika.