Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Miyambi 15:10-15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

10. Wosiya njira adzalangidwa mowawa;Wakuda cidzudzulo adzafa.

11. Kumanda ndi kucionongeko kuli pamaso pa Yehova;Koposa kotani nanga mitima ya ana a anthu?

12. Wonyoza sakonda kudzudzulidwa,Samapita kwa anzeru.

13. Mtima wokondwa usekeretsa nkhope;Koma moyo umasweka ndi zowawa za m'mtima.

14. Mtima wa wozindikira ufunitsa kudziwa;Koma m'kamwa mwa opusa mudya utsiru.

15. Masiku onse a wosauka ali oipa;Koma wokondwera mtima ali ndi phwando losatha.

Werengani mutu wathunthu Miyambi 15