1. Mayankhidwe ofatsa abweza mkwiyo;Koma mau owawitsa aputa msunamo.
2. Lilime la anzeru linena bwino zomwe adziwa;Koma m'kamwa mwa opusa mutsanulira utsiru.
3. Maso a Yehova ali ponseponse,Nayang'anira oipa ndi abwino.
4. Kuciza lilime ndiko mtengo wa moyo;Koma likakhota liswa moyo.