16. Yense wocenjera amacita mwanzeru:Koma wopusa aonetsa utsiru.
17. Mthenga wolakwa umagwa m'zoipa;Koma mtumiki wokhulupirika alamitsa.
18. Wokana mwambo adzasauka nanyozedwa;Koma wolabadira cidzudzulo adzalemekezedwa.
19. Cifuniro cikondweretsa moyo citacitidwa;Koma kusiya zoipa kunyansa opusa,
20. Ukayenda ndi anzeru udzakhala wanzeru:Koma mnzao wa opusa adzaphwetekedwa.