14. Malamulo a wanzeru ndiwo kasupe wa moyo,Apatutsa ku misampha ya imfa.
15. Nzeru yabwino ipatsa cisomo;Koma njira ya aciwembu iri makolokoto.
16. Yense wocenjera amacita mwanzeru:Koma wopusa aonetsa utsiru.
17. Mthenga wolakwa umagwa m'zoipa;Koma mtumiki wokhulupirika alamitsa.
18. Wokana mwambo adzasauka nanyozedwa;Koma wolabadira cidzudzulo adzalemekezedwa.