13. M'kulakwa kwa milomo muli msampha woipa;Koma wolungama amaturuka m'mabvuto.
14. Munthu amakhuta zabwino ndi zipatso za m'kamwa mwace;Zocita za manja ace zidzabwezedwa kwa iye.
15. Njira ya citsiru nlolungama pamaso pace pace;Koma wanzeru amamvera uphungu.