Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Miyambi 11:27-31 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

27. Wopwaira ubwino afunitsa cikondwerero;Koma zoipa zidzamfikira wozilondola.

28. Wokhulupmra cuma cace adzagwa;Koma olungama adzaphuka ngati tsamba.

29. Wobvuta banja lace adzalowa m'zomsautsa;Wopusa adzatumikira wanzeru.

30. Cipatso ca wolungama ndi mtengo wa moyo;Ndipo wokola mtima ali wanzeru.

31. Taonani, wolungama adzalandira mphotho kunja kuno;Koposa kotani woipa ndi wocimwa?

Werengani mutu wathunthu Miyambi 11