Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Miyambi 1:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. MIYAMBI ya Solomo mwana wa Davide, mfumu ya Israyeli.

2. Kudziwa nzeru ndi mwambo;Kuzindikira mau ozindikiritsa;

Werengani mutu wathunthu Miyambi 1