Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mika 7:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Manja ao onse awiri agwira coipa kucicita ndi cangu; kalonga apempha, ndi woweruza aweruza cifukwa ca mphotho; ndi wamkuruyo angonena cosakaza moyo wace; ndipo aciluka pamodzi.

Werengani mutu wathunthu Mika 7

Onani Mika 7:3 nkhani