Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mika 7:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Adzanyambita pfumbi ngati njoka; ngati zokwawa za padziko, adzanjenjemera poturuka m'ngaka mwao; adzafika kwa Yehova Mulungu wao ndi mantha, nadzaopa cifukwa ca iwe.

Werengani mutu wathunthu Mika 7

Onani Mika 7:17 nkhani