Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mika 5:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo, otsala a Yakobo adzakhala mwa amitundu, pakati pa mitundu yambiri ya anthu, ngati mkango mwa nyama za kuthengo, ngati msona wa mkango mwa magulu a nkhosa; umenewo ukapitako, upondereza, numwetula, ndipo palibe wakupulumutsa.

Werengani mutu wathunthu Mika 5

Onani Mika 5:8 nkhani