Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mika 5:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ameneyo adzakhala Mtendere; pamene a ku Asuri adzalowa m'dziko lathu, ndi pamene adzaponda m'zinyumba zathu, tidzawaukitsira abusa asanu ndi awiri, ndi akalonga asanu ndi atatu.

Werengani mutu wathunthu Mika 5

Onani Mika 5:5 nkhani