Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mika 2:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kodi adzati, Nyumba ya Yakobo iwe, Mzimu wa Yehova waperewera kodi? izi ndi nchito zace kodi? Mau anga samcitira zokoma kodi, iye amene ayenda coongoka?

Werengani mutu wathunthu Mika 2

Onani Mika 2:7 nkhani